Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ana ako aamuna ndi ana ako aakazi adzaperekedwa kwa anthu ena+ iwe ukuona ndipo udzawalakalaka nthawi zonse, koma manja ako adzakhala opanda mphamvu.+

  • Deuteronomo 32:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kunja lupanga lidzawasandutsa anamfedwa,+

      Ndipo mkati mwa nyumba, mantha adzawasandutsa anamfedwa.+

      Zimenezi zidzawaphera anyamata ndi anamwali,+

      Mwana woyamwa pamodzi ndi munthu wa imvi.+

  • Yeremiya 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndipeta anthu anga ngati mbewu kuzipata za m’dzikoli. Ndithu, ndiwauluza ndi chifoloko.+ Ndiwaphera ana awo+ ndipo ndiwononga anthu anga chifukwa sanasiye kuchita zinthu zoipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena