Salimo 10:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 N’chifukwa chiyani woipa amanyoza Mulungu?+Mumtima mwake amati: “Simudzandiimba mlandu.”+ Mlaliki 8:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Popeza anthu ochita zoipa sanalangidwe msanga,+ n’chifukwa chake mtima wa ana a anthu wakhazikika pa kuchita zoipa.+ Yesaya 56:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 “Tabwerani amuna inu! Dikirani kaye ndikatenge vinyo. Timwe mpaka kuledzera.+ Mawa lidzakhalanso ngati lero, mwinanso kuposa pamenepa.”+ Ezekieli 12:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 “Iwe mwana wa munthu, a nyumba ya Isiraeli akunena kuti, ‘Masomphenya amene akuona adzachitika m’tsogolo, ndipo akulosera zinthu zimene zidzachitike m’tsogolo kwambiri.’+ 2 Petulo 3:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 amene azidzati:+ “Kukhalapo* kwake kolonjezedwa kuja kuli kuti?+ Taonani, kuchokera tsiku limene makolo athu anamwalira, zinthu zonse zikupitirirabe chimodzimodzi ngati mmene zakhalira kuyambira pa chiyambi cha chilengedwe.”+
11 Popeza anthu ochita zoipa sanalangidwe msanga,+ n’chifukwa chake mtima wa ana a anthu wakhazikika pa kuchita zoipa.+
12 “Tabwerani amuna inu! Dikirani kaye ndikatenge vinyo. Timwe mpaka kuledzera.+ Mawa lidzakhalanso ngati lero, mwinanso kuposa pamenepa.”+
27 “Iwe mwana wa munthu, a nyumba ya Isiraeli akunena kuti, ‘Masomphenya amene akuona adzachitika m’tsogolo, ndipo akulosera zinthu zimene zidzachitike m’tsogolo kwambiri.’+
4 amene azidzati:+ “Kukhalapo* kwake kolonjezedwa kuja kuli kuti?+ Taonani, kuchokera tsiku limene makolo athu anamwalira, zinthu zonse zikupitirirabe chimodzimodzi ngati mmene zakhalira kuyambira pa chiyambi cha chilengedwe.”+