Mateyu 24:44 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 44 Pa chifukwa chimenechi, nanunso khalani okonzeka,+ chifukwa pa ola limene simukuliganizira, Mwana wa munthu adzabwera. Mateyu 25:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 “Chotero khalanibe maso+ chifukwa simukudziwa tsiku kapena ola lake.+ Maliko 13:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ndipo anthu onse adzadana nanu chifukwa cha dzina langa.+ Koma amene adzapirire mpaka pa mapeto,+ ndiye amene adzapulumuke.+ 2 Petulo 3:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Muzichita zimenezi poyembekezera+ ndi kukumbukira nthawi zonse kukhalapo kwa tsiku la Yehova,+ pamene kumwamba kudzapsa ndi moto n’kusungunuka,+ ndipo zinthu zimene zimapanga kumwamba ndi dziko lapansi zidzatentha kwambiri n’kusungunuka. Chivumbulutso 3:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Choncho, pitiriza kukumbukira zimene unalandira+ ndi zimene unamva. Pitiriza kuzitsatira,+ ndipo ulape.+ Ndithudi, ukapanda kudzuka,+ ndidzabwera ngati mbala,+ ndipo sudzadziwa ngakhale pang’ono ola limene ndidzafike kwa iwe.+
44 Pa chifukwa chimenechi, nanunso khalani okonzeka,+ chifukwa pa ola limene simukuliganizira, Mwana wa munthu adzabwera.
13 Ndipo anthu onse adzadana nanu chifukwa cha dzina langa.+ Koma amene adzapirire mpaka pa mapeto,+ ndiye amene adzapulumuke.+
12 Muzichita zimenezi poyembekezera+ ndi kukumbukira nthawi zonse kukhalapo kwa tsiku la Yehova,+ pamene kumwamba kudzapsa ndi moto n’kusungunuka,+ ndipo zinthu zimene zimapanga kumwamba ndi dziko lapansi zidzatentha kwambiri n’kusungunuka.
3 Choncho, pitiriza kukumbukira zimene unalandira+ ndi zimene unamva. Pitiriza kuzitsatira,+ ndipo ulape.+ Ndithudi, ukapanda kudzuka,+ ndidzabwera ngati mbala,+ ndipo sudzadziwa ngakhale pang’ono ola limene ndidzafike kwa iwe.+