Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 35:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno Yakobo anauza anthu a m’banja lake ndi onse amene anali naye kuti: “Chotsani milungu yachilendo imene ili pakati panu.+ Dziyeretseni ndipo sinthani zovala zanu.+

  • Ekisodo 20:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Usakhale ndi milungu ina iliyonse+ kupatulapo ine.*

  • Ezekieli 20:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “Tsopano uza nyumba ya Isiraeli kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Kodi anthu inu mukudziipitsa potsatira njira za makolo anu?+ Kodi mukutsatira zinthu zawo zonyansa ndi kuchita zachiwerewere ndi mafano amenewo?+

  • 1 Akorinto 8:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ngakhale zili choncho, si onse amene amadziwa zimenezi.+ Koma ena, pokhala ozolowera mafano enaake mpaka panopo, akamadya chakudya choperekedwa kwa fano amachidya monga choperekedwadi kwa fano,+ ndipo popeza chikumbumtima chawo n’chofooka, chimaipitsidwa.+

  • 1 Akorinto 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiye chifukwa chake, okondedwa anga, thawani+ kupembedza mafano.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena