Aefeso 3:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pa chifukwa chimenechi, ine Paulo, ndine wandende+ mwa Khristu Yesu m’malo mwa inu, anthu a mitundu ina+ . . . Afilipi 1:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Moti, kumangidwa kwanga+ chifukwa cha Khristu, kwadziwika ndi aliyense+ pakati pa Asilikali Oteteza Mfumu ndi ena onse.+ Akolose 4:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Tsopano landirani moni wanga wolemba ndekha ndi dzanja langa,+ ineyo Paulo. Pitirizani kukumbukira maunyolo+ amene andimanga nawo kundende kuno. Kukoma mtima kwakukulu kukhale nanu. 2 Timoteyo 1:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Chotero, usachite manyazi ndi ntchito yochitira umboni za Ambuye wathu,+ kapena za ineyo amene ndine mkaidi chifukwa cha iye.+ Khala wokonzeka kumva zowawa+ mu mphamvu ya Mulungu+ chifukwa cha uthenga wabwino. Filimoni 13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ndikanakonda kumusunga kuti m’malo mwa iwe,+ apitirize kunditumikira pamene ndili m’ndende+ chifukwa cha uthenga wabwino.
3 Pa chifukwa chimenechi, ine Paulo, ndine wandende+ mwa Khristu Yesu m’malo mwa inu, anthu a mitundu ina+ . . .
13 Moti, kumangidwa kwanga+ chifukwa cha Khristu, kwadziwika ndi aliyense+ pakati pa Asilikali Oteteza Mfumu ndi ena onse.+
18 Tsopano landirani moni wanga wolemba ndekha ndi dzanja langa,+ ineyo Paulo. Pitirizani kukumbukira maunyolo+ amene andimanga nawo kundende kuno. Kukoma mtima kwakukulu kukhale nanu.
8 Chotero, usachite manyazi ndi ntchito yochitira umboni za Ambuye wathu,+ kapena za ineyo amene ndine mkaidi chifukwa cha iye.+ Khala wokonzeka kumva zowawa+ mu mphamvu ya Mulungu+ chifukwa cha uthenga wabwino.
13 Ndikanakonda kumusunga kuti m’malo mwa iwe,+ apitirize kunditumikira pamene ndili m’ndende+ chifukwa cha uthenga wabwino.