Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 130:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Inu mumakhululukiradi,+

      Kuti anthu akuopeni.+

  • Aroma 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma mmene zilili ndi mphatsoyi si mmene zinalili ndi uchimowo. Popeza ngati mwa uchimo wa munthu mmodzi ambiri anafa, kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu ndiponso mphatso yake yaulere zinasefukira kwa anthu ambiri.+ Mphatso yaulere imeneyi inaperekedwa limodzi ndi kukoma mtima kwakukulu kudzera mwa munthu mmodzi,+ Yesu Khristu.

  • Aroma 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa chiyani? Kuti mmene uchimo unalamulira monga mfumu pamodzi ndi imfa,+ momwemonso kukoma mtima kwakukulu+ kulamulire monga mfumu kudzera m’chilungamo. Zimenezi zichitike kuti moyo wosatha+ ubwere kudzera mwa Yesu Khristu Ambuye wathu.

  • Aroma 11:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Choncho taona kukoma mtima+ komanso kusalekerera+ kwa Mulungu. Amene anagwa anaona kusalekerera+ kwake, koma iweyo ukuona kukoma mtima kwa Mulungu, malinga ngati ukukhalabe+ m’kukoma mtima kwake. Apo ayi, iwenso udzadulidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena