Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Afilipi 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Zidzatero mogwirizana n’kuti ndikudikira mwachidwi,+ ndiponso ndili ndi chiyembekezo+ chakuti sindidzachititsidwa manyazi+ mwa njira iliyonse. Koma kuti mwa ufulu wanga wonse wa kulankhula,+ Khristu alemekezedwe mwa thupi langa tsopano, monga mmene zakhala zikuchitikira m’mbuyo monsemu.+ Kaya ndikhala ndi moyo kapena ndimwalira.+

  • 2 Timoteyo 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 N’chifukwa chake ndikuvutika chonchi,+ koma sindikuchita manyazi.+ Pakuti ndikudziwa amene ndikumukhulupirira, ndipo ndikukhulupirira kuti adzasunga+ chimene ndachiika m’manja mwake kufikira tsikulo.+

  • Aheberi 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tichite zimenezi pamene tikuyang’anitsitsa Mtumiki Wamkulu+ ndi Wokwaniritsa chikhulupiriro chathu,+ Yesu. Chifukwa cha chimwemwe chimene anamuikira patsogolo pake,+ anapirira mtengo wozunzikirapo.* Iye sanasamale kuti zochititsa manyazi zimuchitikira, ndipo tsopano wakhala pansi kudzanja lamanja la mpando wachifumu wa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena