Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 13:27, 28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Gawo lawolo linaphatikizaponso mizinda ya mʼchigwa ya Beti-harana, Beti-nimira,+ Sukoti,+ Zafoni ndi dera lotsala la dziko la Mfumu Sihoni ya ku Hesiboni.+ Mtsinje wa Yorodano ndi umene unali malire awo kuchokera kumunsi kwa nyanja ya Kinereti,*+ kumʼmawa kwa mtsinje wa Yorodano. 28 Dera limeneli linali cholowa cha anthu a fuko la Gadi chimene anapatsidwa motsatira mabanja awo. Iwo anapatsidwa derali limodzi ndi mizinda komanso midzi ya kumeneko.

  • Salimo 108:7-9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Popeza ndi woyera,* Mulungu walankhula kuti:

      “Ndidzasangalala popereka Sekemu+ ngati cholowa,

      Ndipo ndidzayezera anthu anga malo mʼchigwa cha Sukoti.+

       8 Giliyadi+ ndi wanga, ngati mmene zilili ndi Manase,

      Ndipo Efuraimu ndi chipewa* choteteza mutu wanga.+

      Yuda akuimira mphamvu zanga zolamula.+

       9 Mowabu ndi beseni langa losambiramo.+

      Edomu ndidzamuponyera nsapato zanga.+

      Ndidzafuula mosangalala chifukwa chogonjetsa Filisitiya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena