Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 31:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Inetu ndikuitana ndi kutchula dzina Bezaleli+ mwana wamwamuna wa Uri, mwana wa Hura wa fuko la Yuda.+

  • Ekisodo 35:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Kenako Mose anauza ana a Isiraeli kuti: “Yehova waitana ndi kutchula dzina Bezaleli,+ mwana wamwamuna wa Uri, mwana wa Hura wa fuko la Yuda.

  • Ekisodo 36:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 “Bezaleli komanso Oholiabu+ ndi mwamuna aliyense wa mtima wanzeru amene Yehova wam’patsa nzeru+ ndi kuzindikira+ pa zinthu zimenezi, ayenera kugwira ntchitoyi. Iwowa apatsidwa nzeru ndi kuzindikira kuti adziwe kuchita ntchito zonse zopatulika motsatira zonse zimene Yehova walamula.”+

  • Ekisodo 37:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Tsopano Bezaleli+ anapanga Likasa+ la mtengo wa mthethe, mikono iwiri ndi hafu m’litali, mkono umodzi ndi hafu m’lifupi, ndi mkono umodzi ndi hafu msinkhu wake.+

  • 2 Mbiri 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndipo guwa lansembe lamkuwa+ limene Bezaleli+ mwana wa Uri mwana wa Hura+ anapanga, anali ataliika patsogolo pa chihema chopatulika cha Yehova. Choncho Solomo ndi mpingowo anafunsira paguwalo monga mwa nthawi zonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena