Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 2:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pamenepo Naomi anauza mpongozi wakeyo kuti: “Yehova amene sanaleke kusonyeza kukoma mtima kosatha+ kwa amoyo ndi akufa,+ am’dalitse munthu ameneyu.”+ Ndipo Naomi anapitiriza kuti: “Munthuyutu ndi wachibale wathu.+ Ndi mmodzi wa otiwombola.”+

  • Rute 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiye ine ndaganiza zoti ndikuuze kuti, ‘Ugule mundawo+ pamaso pa anthu ndi pamaso pa akulu a mzinda uno.+ Ngati ukufuna kuuwombola, uwombole. Koma ngati sukufuna undiuze kuti ndidziwe, popeza palibenso wina amene angauwombole koma iweyo,+ pambuyo pako pali ine.’” Pamenepo, wowombola uja anati: “Ndiuwombola ineyo.”+

  • Rute 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Poyankha wowombolayo anati: “Sinditha kuuwombola, kuopera kuti ndingawononge cholowa changa. Iweyo uuwombole m’malo mwa ine, chifukwa ine sinditha kuuwombola.”

  • Yeremiya 32:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 ‘Kukubwera Hanameli mwana wa Salumu m’bale wa bambo ako, kudzakuuza kuti: “Ugule munda wanga wa ku Anatoti+ chifukwa iweyo ndi amene uli ndi ufulu wogula mundawo.”’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena