Ekisodo 29:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Utenge mafuta+ onse okuta matumbo,+ mafuta a pachiwindi,*+ impso ziwiri ndi mafuta ake, n’kuzitentha* paguwa lansembe.+ Levitiko 3:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pamenepo azipereka mbali ina ya nsembe yachiyanjanoyo monga nsembe yotentha ndi moto yoperekedwa kwa Yehova. Azipereka mafuta+ okuta matumbo, mafuta onse amene ali pamatumbo.+ Levitiko 6:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ndipo moto wa paguwa lansembe uziyaka nthawi zonse. Usamazime. Wansembe aziponyapo nkhuni+ m’mawa uliwonse ndi kuikapo nsembe yopsereza pankhunipo. Akatero, azitentha mafuta a nsembe yachiyanjano pamotopo.+ Levitiko 9:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndipo mafuta,+ impso ndi mafuta a pachiwindi zimene anazitenga panyama ya nsembe yamachimo anazitentha paguwa lansembe,+ monga mmene Yehova analamulira Mose.
13 Utenge mafuta+ onse okuta matumbo,+ mafuta a pachiwindi,*+ impso ziwiri ndi mafuta ake, n’kuzitentha* paguwa lansembe.+
3 Pamenepo azipereka mbali ina ya nsembe yachiyanjanoyo monga nsembe yotentha ndi moto yoperekedwa kwa Yehova. Azipereka mafuta+ okuta matumbo, mafuta onse amene ali pamatumbo.+
12 Ndipo moto wa paguwa lansembe uziyaka nthawi zonse. Usamazime. Wansembe aziponyapo nkhuni+ m’mawa uliwonse ndi kuikapo nsembe yopsereza pankhunipo. Akatero, azitentha mafuta a nsembe yachiyanjano pamotopo.+
10 Ndipo mafuta,+ impso ndi mafuta a pachiwindi zimene anazitenga panyama ya nsembe yamachimo anazitentha paguwa lansembe,+ monga mmene Yehova analamulira Mose.