Levitiko 16:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Koma mbuzi imene maere asonyeza kuti ndi ya Azazeli, aziiimika yamoyo pamaso pa Yehova kuti aiphimbire machimo. Akatero aziitumiza+ m’chipululu monga ya Azazeli.+ Salimo 103:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Monga mmene kum’mawa kwatalikirana ndi kumadzulo,+Momwemonso, watiikira kutali zolakwa zathu.+ Ezekieli 18:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Zolakwa zonse zimene anachita sizidzakumbukiridwa ndipo sadzalangidwa nazo.+ Adzakhalabe ndi moyo chifukwa cha zinthu zolungama zimene anachita.’+ Mika 7:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Inu mudzatichitiranso chifundo+ ndipo mudzapondaponda zolakwa zathu.+ Machimo athu onse mudzawaponya pakati pa nyanja yozama.+ Aheberi 13:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Zinalinso chimodzimodzi ndi Yesu. Kuti ayeretse+ anthu ndi magazi ake,+ anakavutikira kunja kwa chipata.+
10 Koma mbuzi imene maere asonyeza kuti ndi ya Azazeli, aziiimika yamoyo pamaso pa Yehova kuti aiphimbire machimo. Akatero aziitumiza+ m’chipululu monga ya Azazeli.+
22 Zolakwa zonse zimene anachita sizidzakumbukiridwa ndipo sadzalangidwa nazo.+ Adzakhalabe ndi moyo chifukwa cha zinthu zolungama zimene anachita.’+
19 Inu mudzatichitiranso chifundo+ ndipo mudzapondaponda zolakwa zathu.+ Machimo athu onse mudzawaponya pakati pa nyanja yozama.+
12 Zinalinso chimodzimodzi ndi Yesu. Kuti ayeretse+ anthu ndi magazi ake,+ anakavutikira kunja kwa chipata.+