2 Samueli 8:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Davide anagonjetsanso Amowabu+ ndi kuwayeza ndi chingwe. Iye anawagoneka pansi kuti ayeze zingwe ziwiri ndi kuwapha, ndiponso chingwe chimodzi chathunthu n’kuwasiya amoyo.+ Choncho Amowabu anakhala atumiki a Davide+ ndipo anali kukhoma msonkho kwa iye.+ 1 Mbiri 18:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Kenako anagonjetsa Mowabu,+ moti Amowabuwo anakhala atumiki a Davide ndipo anali kukhoma msonkho kwa iye.+ Salimo 108:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Mowabu+ ndi beseni langa losambiramo.+Ndidzaponyera Edomu+ nsapato zanga.+Ndidzafuula mosangalala+ chifukwa chogonjetsa Filisitiya.”+ Salimo 110:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Adzapereka chiweruzo pakati pa anthu a mitundu ina.+Adzachititsa mitembo ya anthu kupezeka paliponse.+Adzaphwanyaphwanya mtsogoleri wa dziko la anthu ambiri.+ Yeremiya 48:45 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 45 ‘Anthu othawa aima chilili mumthunzi wa Hesiboni ndipo alibe mphamvu. Moto udzachokera ku Hesiboni+ ndipo malawi a moto adzachokera ku Sihoni+ ndi kutentha Mowabu m’mutu, m’mphepete mwa makutu, komanso paliwombo pa ana osokoneza.’+
2 Davide anagonjetsanso Amowabu+ ndi kuwayeza ndi chingwe. Iye anawagoneka pansi kuti ayeze zingwe ziwiri ndi kuwapha, ndiponso chingwe chimodzi chathunthu n’kuwasiya amoyo.+ Choncho Amowabu anakhala atumiki a Davide+ ndipo anali kukhoma msonkho kwa iye.+
2 Kenako anagonjetsa Mowabu,+ moti Amowabuwo anakhala atumiki a Davide ndipo anali kukhoma msonkho kwa iye.+
9 Mowabu+ ndi beseni langa losambiramo.+Ndidzaponyera Edomu+ nsapato zanga.+Ndidzafuula mosangalala+ chifukwa chogonjetsa Filisitiya.”+
6 Adzapereka chiweruzo pakati pa anthu a mitundu ina.+Adzachititsa mitembo ya anthu kupezeka paliponse.+Adzaphwanyaphwanya mtsogoleri wa dziko la anthu ambiri.+
45 ‘Anthu othawa aima chilili mumthunzi wa Hesiboni ndipo alibe mphamvu. Moto udzachokera ku Hesiboni+ ndipo malawi a moto adzachokera ku Sihoni+ ndi kutentha Mowabu m’mutu, m’mphepete mwa makutu, komanso paliwombo pa ana osokoneza.’+