Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 22:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma Mulungu anauza Balamu kuti: “Usapite nawo, ndipo anthuwo usakawatemberere,+ pakuti iwo ndi odalitsidwa.”+

  • Numeri 24:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Tsopano Balamu ananyamuka kumabwerera kwawo.+ Nayenso Balaki ananyamuka kulowera njira yake.

  • Yoswa 13:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pakati pa anthu amene ana a Isiraeli anawapha ndi lupanga, panali Balamu mwana wa Beori,+ wolosera zam’tsogolo+ uja.

  • 2 Petulo 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Popeza anasiya njira yowongoka, asocheretsedwa. Atsatira njira ya Balamu+ mwana wa Beori, amene anakonda mphoto ya kuchita zoipa,+

  • Yuda 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tsoka kwa iwo, chifukwa chakuti ayenda m’njira ya Kaini.+ Athamangira m’njira yolakwika ya Balamu+ kuti alandire mphoto, ndipo awonongeka potengera kulankhula kopanduka+ kwa Kora.+

  • Chivumbulutso 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “‘Koma ngakhale zili choncho, ndakupeza ndi milandu ingapo. Iwe kumeneko uli ndi anthu olimbikira chiphunzitso cha Balamu,+ amene anaphunzitsa Balaki+ kuikira ana a Isiraeli chopunthwitsa kuti adye zoperekedwa nsembe kwa mafano ndi kuchita dama.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena