Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno amuna a ku Efuraimu anasonkhana pamodzi n’kuwolokera tsidya lina chakumpoto, ndi kuuza Yefita kuti: “N’chifukwa chiyani unawoloka kukamenya ndi ana a Amoni ife osatiitana kuti tipite nawe?+ Tikutentha ndi moto pamodzi ndi nyumba yako.”+

  • 2 Samueli 19:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Pamenepo anthu onse a Isiraeli anabwera kwa mfumu ndi kuiuza kuti: “N’chifukwa chiyani+ abale athu a ku Yuda akubweretsani mozemba inu mfumu Davide, pamodzi ndi banja lanu ndi anthu onse amene anali ndi inu kutsidya la Yorodano?”+

  • 2 Mbiri 25:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chotero Amaziya anapatula asilikali amene anabwera kwa iye kuchokera ku Efuraimu n’kuwauza kuti abwerere kwawo. Koma asilikaliwo anawakwiyira kwambiri Ayuda moti anabwerera kwawo ali okwiya kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena