Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Nyamukani,+ inu Yehova! Ndipulumutseni+ inu Mulungu wanga!+

      Pakuti mudzakantha adani anga onse pachibwano.+

      Mano a anthu oipa mudzawaphwanyaphwanya.+

  • Salimo 18:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Kodi pali Mulungu winanso woposa Yehova?+

      Kodi pali thanthwe linanso loposa Mulungu wathu?+

  • Salimo 44:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti iwo sanatenge dzikolo chifukwa cha lupanga lawo,+

      Ndipo si mkono wawo umene unawabweretsera chipulumutso.+

      Koma chinabwera ndi dzanja lanu lamanja,+ mkono wanu ndi kuwala kwa nkhope yanu,

      Chifukwa munakondwera nawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena