Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 31:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pa nthawiyi n’kuti Labani atapita kukameta ubweya wa nkhosa zake. Akali kumeneko, Rakele anaba aterafi*+ a bambo ake.

  • Oweruza 18:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno amuna asanu amene anapita kukazonda+ dziko la Laisi+ aja, anauza abale awo kuti: “Kodi mukudziwa kuti m’nyumba izi muli efodi, aterafi,+ chifaniziro chosema+ ndi chifaniziro chopangidwa ndi chitsulo chosungunula?+ Ndiyetu dziwani chochita.”+

  • Hoseya 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ziyenera kukhala choncho chifukwa chakuti kwa masiku ambiri, ana a Isiraeli adzakhala opanda mfumu,+ kalonga, nsembe,+ chipilala chopatulika, efodi,+ ndi aterafi.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena