Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Asakhale m’dziko lako, kuti asakuchimwitse pamaso panga. Ukatumikira milungu yawo, umenewo udzakhala msampha kwa iwe.”+

  • Ekisodo 34:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Samalani kuti musachite pangano ndi anthu a m’dziko limene mukupitako+ kuopera kuti ungakhale msampha pakati panu.+

  • Deuteronomo 7:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Muwononge anthu a mitundu yonse amene Yehova Mulungu wanu akuwapereka kwa inu.+ Musawamvere chisoni+ ndipo musatumikire milungu yawo+ chifukwa kuchita zimenezo kudzakutcherani msampha.+

  • 1 Mafumu 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Akaziwa anali ochokera m’mitundu imene Yehova anauza ana a Isiraeli kuti: “Musamapite pakati pawo+ ndipo iwonso asamabwere pakati panu, chifukwa ndithu adzapotoza mitima yanu kuti itsatire milungu yawo.”+ Amenewa ndi amene Solomo anaumirira+ kuwakonda.

  • Salimo 78:58
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 58 Iwo anapitiriza kumukhumudwitsa ndi malo awo okwezeka,+

      Ndipo anamuchititsa nsanje ndi zifaniziro zawo zogoba.+

  • Salimo 106:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Anayamba kutumikira mafano awo,+

      Ndipo mafanowo anakhala msampha wawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena