Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 25:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo Nabala anayankha atumiki a Davide kuti: “Kodi Davide ndani,+ ndipo mwana wa Jese ndani? Masiku ano atumiki amene akuthawa ambuye awo achuluka kwabasi.+

  • Salimo 35:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Adani anga amandibwezera zoipa m’malo mwa zabwino,+

      Ndipo ndimakhala wachisoni ngati wofedwa.+

  • Salimo 38:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iwo anali kundibwezera choipa m’malo mwa chabwino,+

      Ndikamayesetsa kuchita chabwino anali kunditsutsa.+

  • Salimo 109:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndikawachitira zabwino amandibwezera zoipa,+

      Ndikawasonyeza chikondi amandibwezera chidani.+

  • Miyambo 17:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Aliyense wobwezera zoipa pa zabwino,+ zoipa sizidzachoka panyumba pake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena