-
Yohane 10:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 Yesu anawauza kuti: “Ndakuonetsani ntchito zambiri zabwino zochokera kwa Atate. Tsopano mukundiponya miyala chifukwa cha ntchito iti mwa zimenezi?”
-
-
Yohane 18:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Yesu anamuyankha kuti: “Ngati ndalankhula molakwika, pereka umboni wa cholakwikacho. Koma ngati ndalankhula moyenera, n’chifukwa chiyani ukundimenya?”
-