Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 1:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Atatero anthuwo anayamba kumulondola ndipo anali kuimba zitoliro+ ndi kusangalala kwambiri,+ moti nthaka+ inang’ambika chifukwa cha phokoso lawo.

  • 2 Mafumu 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atafika anaona mfumu itaimirira pafupi ndi chipilala+ malinga ndi mwambo wawo. Anaonanso atsogoleri a asilikali ndi anthu oimba malipenga+ ali pafupi ndi mfumuyo, ndipo anthu onse a m’dzikolo anali kusangalala+ ndi kuimba malipenga. Nthawi yomweyo Ataliya+ anang’amba zovala zake n’kuyamba kukuwa kuti: “Mwandichitira chiwembu! Mwandichitira chiwembu!”+

  • 1 Mbiri 12:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Ndiponso anthu onse apafupi ndi kumeneko, mpaka kumadera a Isakara,+ Zebuloni,+ ndi Nafitali,+ anali kubweretsa chakudya pa abulu,+ ngamila, nyulu* ndi ng’ombe. Anabweretsa zakudya zophikidwa ndi ufa.+ Anabweretsanso nkhuyu zouma zoumba pamodzi,+ mphesa zouma zoumba pamodzi,+ vinyo,+ mafuta,+ ng’ombe,+ ndi nkhosa.+ Anabweretsa zimenezi zambirimbiri, popeza mu Isiraeli munali chisangalalo+ chachikulu.

  • Chivumbulutso 19:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako ndinamva mawu ngati a khamu lalikulu, omveka ngati mkokomo wa madzi ambiri ndi mabingu amphamvu. Mawuwo anati: “Tamandani Ya,+ anthu inu, chifukwa Yehova* Mulungu wathu, Wamphamvuyonse,+ wayamba kulamulira monga mfumu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena