Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pakuti amadzinyenga yekha,+

      Ndipo sazindikira cholakwa chake ndi kudana nacho.+

  • Salimo 125:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Koma anthu obwerera kunjira zawo zokhotakhota,+

      Yehova adzawapereka ku chilango pamodzi ndi ochita zopweteka anzawo.+

      Ndipo mu Isiraeli mudzakhala mtendere.+

  • Mlaliki 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mwana wosauka koma wanzeru ali bwino+ kuposa mfumu yokalamba koma yopusa,+ imene sionanso kufunika kochenjezedwa.+

  • Malaki 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kuyambira m’masiku a makolo anu mwakhala mukupatuka pa malamulo anga ndipo simunawasunge.+ Bwererani kwa ine ndipo ine ndibwerera kwa inu,”+ watero Yehova wa makamu.

      Koma inu mukunena kuti: “Tibwerere motani?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena