1 Samueli 14:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndiyeno tsiku lina zinachitika kuti Yonatani+ mwana wa Sauli anauza mtumiki wake womunyamulira zida kuti: “Tiye tiwolokere kumudzi wa asilikali a Afilisiti umene uli patsidyapo.” Koma Yonatani sanauze bambo ake zimenezi.+ 1 Samueli 14:49 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 49 Ana aamuna a Sauli anali Yonatani,+ Isivi ndi Malikisuwa.+ Ndipo mayina a ana ake awiri aakazi ndi awa: Woyamba kubadwa anali Merabu,+ ndipo wamng’ono anali Mikala.+ 2 Samueli 1:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Kenako Davide anamufunsa kuti: “Zayenda bwanji kumeneko? Chonde, ndiuze.” Iye anayankha kuti: “Anthu athawa kunkhondo komanso anthu ambiri agwa ndipo afa,+ ngakhalenso Sauli+ ndi mwana wake Yonatani+ afa.”
14 Ndiyeno tsiku lina zinachitika kuti Yonatani+ mwana wa Sauli anauza mtumiki wake womunyamulira zida kuti: “Tiye tiwolokere kumudzi wa asilikali a Afilisiti umene uli patsidyapo.” Koma Yonatani sanauze bambo ake zimenezi.+
49 Ana aamuna a Sauli anali Yonatani,+ Isivi ndi Malikisuwa.+ Ndipo mayina a ana ake awiri aakazi ndi awa: Woyamba kubadwa anali Merabu,+ ndipo wamng’ono anali Mikala.+
4 Kenako Davide anamufunsa kuti: “Zayenda bwanji kumeneko? Chonde, ndiuze.” Iye anayankha kuti: “Anthu athawa kunkhondo komanso anthu ambiri agwa ndipo afa,+ ngakhalenso Sauli+ ndi mwana wake Yonatani+ afa.”