Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 35:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “‘Ngati munthu wamenya mnzake ndi chitsulo, mnzakeyo n’kufa, ameneyo ndi wakupha munthu.+ Ndipo wakupha munthuyo ayenera kuphedwa ndithu.+

  • 2 Samueli 3:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Abineri atabwerera ku Heburoni,+ Yowabu anam’tengera pambali kuchipata kuti alankhulane naye pa awiri.+ Koma kumeneko anamubaya pamimba+ moti anafa chifukwa chokhetsa magazi a Asaheli,+ m’bale wake wa Yowabu.

  • 1 Mafumu 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Iweyo ukudziwa bwino kwambiri zimene Yowabu mwana wa Zeruya anandichita,+ mwa kupha akulu awiri a asilikali a Isiraeli, Abineri+ mwana wa Nera ndi Amasa+ mwana wa Yeteri.+ Mwakutero, anakhetsa magazi+ ankhondo pa nthawi yamtendere. Ndipo anadetsa ndi magazi ankhondo lamba amene anali m’chiuno mwake ndiponso nsapato zimene zinali kuphazi kwake.

  • Salimo 55:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma inu Mulungu, mudzatsitsira oipa kumanda.+

      Ndipo anthu amene ali ndi mlandu wa magazi komanso anthu achinyengo, sadzakwanitsa kukhala ngakhale hafu ya moyo wawo.+

      Koma ine ndidzakhulupirira inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena