Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno Yaeli mkazi wa Hiberi anatenga chikhomo cha hema ndi nyundo. Kenako analowa m’hemamo, akuyenda monyang’ama n’kukhoma chikhomocho m’mutu mwa Sisera pafupi ndi khutu,+ mpaka chikhomocho chinalowa pansi. Apa n’kuti Sisera ali m’tulo tofa nato ndiponso ali wotopa kwambiri. Mmenemu ndi mmene Sisera anafera.+

  • Oweruza 5:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Inu Yehova, adani anu onse afafanizidwe chimodzimodzi,+

      Ndipo okukondani inu+ akhale amphamvu ngati mmene dzuwa limakhalira.”+

      Choncho, dzikolo linakhala pa mtendere zaka 40.+

  • Salimo 45:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mivi yako yakuthwa idzalasa mitima ya adani a mfumu,+

      Mitundu ya anthu idzagwa pamapazi ako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena