Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 22:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Yehosafati anali ndi zaka 35 pamene anayamba kulamulira. Iye analamulira ku Yerusalemu zaka 25. Mayi ake dzina lawo linali Azuba mwana wa Sili.

  • 2 Mbiri 17:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iye anafunafuna Mulungu wa bambo ake+ ndipo anayenda+ motsatira chilamulo chake, sanatsatire zochita za Aisiraeli.+

  • 2 Mbiri 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehosafati anakhala ndi chuma chambiri ndi ulemerero waukulu,+ koma anachita mgwirizano wa ukwati+ ndi Ahabu.+

  • 2 Mbiri 19:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Yehosafati anapitiriza kukhala ku Yerusalemu. Iye anayambanso kupita pakati pa anthu, kuyambira ku Beere-seba+ mpaka kudera lamapiri la Efuraimu,+ kuti awabwezere kwa Yehova Mulungu wa makolo awo.+

  • 2 Mbiri 20:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Choncho Yehosafati ndi anthu ake anapita kukafunkha+ zinthu zimene adaniwo anali nazo. Iwo anapeza zinthu zochuluka pakati pa anthuwo monga katundu wosiyanasiyana, zovala ndi zinthu zina zabwinozabwino. Chotero anayamba kutenga zinthuzo mpaka zinawakanika kunyamula.+ Kwa masiku atatu anakhala akututa zofunkhazo chifukwa zinalipo zambiri.

  • Mateyu 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Asa anabereka Yehosafati.+

      Yehosafati anabereka Yehoramu.+

      Yehoramu anabereka Uziya.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena