Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Uziopa Yehova Mulungu wako+ ndi kum’tumikira,+ ndipo uzilumbira pa dzina lake.+

  • 1 Samueli 19:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Sauli anamvera mawu a Yonatani, ndipo analumbira kuti: “Pali Yehova, Mulungu wamoyo,+ Davide saphedwa.”

  • 1 Mafumu 22:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma Mikaya anati: “Pali Yehova Mulungu wamoyo,+ zimene Yehova anene kwa ine n’zimene ndikalankhule.”+

  • 2 Mafumu 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Elisa anayankha kuti: “Pali Yehova wa makamu Mulungu wamoyo amene ndimam’tumikira,+ pakanakhala kuti palibe Yehosafati mfumu ya Yuda, sindikanakuyang’anani+ n’komwe kapena kukusamalani.+

  • Yeremiya 12:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Ndiyeno anthu a mitundu ina akadzaphunzira njira za anthu anga ndi kulumbira m’dzina langa+ kuti, ‘Pali Yehova Mulungu wamoyo!’ monga mmene iwo anaphunzitsira anthu anga kulumbira m’dzina la Baala,+ anthu a mitundu inawo adzakhazikika pakati pa anthu anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena