Salimo 18:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Pakuti ndasunga njira za Yehova,+Sindinachoke kwa Mulungu wanga. Ndikanatero, ndikanachita chinthu choipa.+ Salimo 71:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Inu Mulungu, mwandiphunzitsa kuyambira pa unyamata wanga,+Ndipo mpaka pano ndikunena za ntchito zanu zodabwitsa.+ Miyambo 8:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Kuopa Yehova kumatanthauza kudana ndi zoipa.+ Ndimadana ndi kudzikweza, kunyada,+ njira yoipa ndiponso pakamwa ponena zopotoka.+ Mlaliki 7:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Ndi bwino kuti usunge malangizo oyambawo, ndipo usasiye malangizo achiwiriwo.+ Pakuti munthu amene amaopa Mulungu adzamvera malangizo onsewa.+ Mlaliki 12:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Kumbukira Mlengi wako Wamkulu+ masiku a unyamata wako,+ asanafike masiku oipa+ komanso zisanafike zaka zimene udzati: “Moyo sukundisangalatsa.”+ Yesaya 50:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndani pakati panu amene amaopa+ Yehova ndi kumvera mawu a mtumiki wake?+ Ndani amayenda mu mdima wokhawokha+ ndipo alibe kuwala? Iye akhulupirire dzina la Yehova+ ndipo adalire Mulungu wake.+
21 Pakuti ndasunga njira za Yehova,+Sindinachoke kwa Mulungu wanga. Ndikanatero, ndikanachita chinthu choipa.+
17 Inu Mulungu, mwandiphunzitsa kuyambira pa unyamata wanga,+Ndipo mpaka pano ndikunena za ntchito zanu zodabwitsa.+
13 Kuopa Yehova kumatanthauza kudana ndi zoipa.+ Ndimadana ndi kudzikweza, kunyada,+ njira yoipa ndiponso pakamwa ponena zopotoka.+
18 Ndi bwino kuti usunge malangizo oyambawo, ndipo usasiye malangizo achiwiriwo.+ Pakuti munthu amene amaopa Mulungu adzamvera malangizo onsewa.+
12 Kumbukira Mlengi wako Wamkulu+ masiku a unyamata wako,+ asanafike masiku oipa+ komanso zisanafike zaka zimene udzati: “Moyo sukundisangalatsa.”+
10 Ndani pakati panu amene amaopa+ Yehova ndi kumvera mawu a mtumiki wake?+ Ndani amayenda mu mdima wokhawokha+ ndipo alibe kuwala? Iye akhulupirire dzina la Yehova+ ndipo adalire Mulungu wake.+