Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Usapereke umboni wonamizira mnzako.+

  • Deuteronomo 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “‘Usapereke umboni wonamizira mnzako.+

  • Miyambo 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 mboni yachinyengo yonena mabodza,+ ndi aliyense woyambitsa mikangano pakati pa abale.+

  • Miyambo 24:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Usakhale mboni yotsutsana ndi mnzako popanda umboni,+ chifukwa ukhoza kukhala wopusa ndi milomo yako.+

  • Yesaya 32:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Munthu wakhalidwe loipayo, njira zake n’zoipa.+ Iye amakonza zochita khalidwe lotayirira,+ n’cholinga choti apweteke anthu ozunzika pogwiritsa ntchito mawu abodza,+ ngakhale pamene munthu wosauka akunena zoona.

  • Machitidwe 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kumeneko anabweretsa mboni zonama,+ zimene zinati: “Munthu uyu sakuleka kulankhula mawu onyoza malo oyera ano ndi Chilamulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena