Ekisodo 19:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndipo Yehova anauza Mose kuti: “Pita kwa anthu, uwayeretse lero ndi mawa, ndipo achape zovala zawo.+ Numeri 8:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Aleviwo anadziyeretsa+ n’kuchapa zovala zawo. Pambuyo pake, Aroni anawauza kuti ayende uku ndi uku monga nsembe yoweyula pamaso pa Yehova.+ Kenako Aroniyo anawaphimbira machimo awo kuti awayeretse.+ 2 Mbiri 29:34 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 34 Koma ansembe+ anali ochepa kwambiri ndipo sanathe kusenda nyama zonse za nsembe zopsereza.+ Choncho abale awo+ Alevi anawathandiza mpaka ntchitoyo inatha+ ndiponso kufikira pamene ansembewo anadziyeretsa,+ popeza Alevi ankafunitsitsa kudziyeretsa kuposa ansembe.+ 2 Mbiri 30:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Hezekiya mfumu ya Yuda anapereka+ ku mpingowo ng’ombe zamphongo 1,000 ndi nkhosa 7,000. Akalonganso+ anapereka ku mpingowo ng’ombe zamphongo 1,000 ndi nkhosa 10,000, ndipo ansembe+ ambiri anali kudziyeretsa.
10 Ndipo Yehova anauza Mose kuti: “Pita kwa anthu, uwayeretse lero ndi mawa, ndipo achape zovala zawo.+
21 Aleviwo anadziyeretsa+ n’kuchapa zovala zawo. Pambuyo pake, Aroni anawauza kuti ayende uku ndi uku monga nsembe yoweyula pamaso pa Yehova.+ Kenako Aroniyo anawaphimbira machimo awo kuti awayeretse.+
34 Koma ansembe+ anali ochepa kwambiri ndipo sanathe kusenda nyama zonse za nsembe zopsereza.+ Choncho abale awo+ Alevi anawathandiza mpaka ntchitoyo inatha+ ndiponso kufikira pamene ansembewo anadziyeretsa,+ popeza Alevi ankafunitsitsa kudziyeretsa kuposa ansembe.+
24 Hezekiya mfumu ya Yuda anapereka+ ku mpingowo ng’ombe zamphongo 1,000 ndi nkhosa 7,000. Akalonganso+ anapereka ku mpingowo ng’ombe zamphongo 1,000 ndi nkhosa 10,000, ndipo ansembe+ ambiri anali kudziyeretsa.