Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 14:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tsopano Asa anayamba kupemphera kwa Yehova Mulungu wake,+ kuti: “Inu Yehova mukafuna kuthandiza, zilibe kanthu kuti anthuwo ndi ambiri kapena ndi opanda mphamvu.+ Tithandizeni Yehova Mulungu wathu chifukwa tikudalira inu,+ ndipo tabwera m’dzina lanu+ kudzamenyana ndi khamuli. Inu Yehova ndinu Mulungu wathu.+ Musalole kuti munthu akuposeni mphamvu.”+

  • 2 Mbiri 18:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Akuluakulu oyang’anira asilikali okwera magaleta aja atangomuona Yehosafati, anaganiza kuti: “Iyi ndiyo mfumu ya Isiraeli.”+ Choncho anatembenuka kuti amenyane naye, koma Yehosafati anayamba kukuwa popempha thandizo,+ ndipo Yehova anamuthandiza.+ Nthawi yomweyo Mulungu anawachititsa kuchoka kwa iye.+

  • Salimo 46:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Mulungu ndiye pothawira pathu ndi mphamvu yathu,+

      Thandizo lopezeka mosavuta pa nthawi ya masautso.+

  • Salimo 50:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pa tsiku la nsautso undiitane.+

      Ine ndidzakulanditsa, ndipo iwe udzandilemekeza.”+

  • Salimo 118:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inandizungulira ngati njuchi,+

      Koma inazima ngati moto wa zitsamba zaminga.+

      Ndinali kuikankhira kutali m’dzina la Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena