Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 17:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iwo anayamba kuphunzitsa+ mu Yuda pogwiritsira ntchito buku la chilamulo cha Yehova.+ Ankayendayenda m’mizinda yonse ya Yuda n’kumaphunzitsa anthu.

  • Nehemiya 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ezara anawerenga+ mokweza bukulo m’bwalo lalikulu limene linali pafupi ndi Chipata cha Kumadzi, kuyambira m’mawa+ mpaka masana. Anali kuwerenga bukuli pamaso pa amuna, akazi ndi ana amene akanatha kumvetsera ndi kuzindikira. Anthu onse anatchera khutu kuti amve+ zimene zinali m’buku la chilamuloli.

  • Malaki 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Wansembe ayenera kuphunzitsa anthu kuti adziwe Mulungu. Anthuwo ayenera kufunafuna kumva chilamulo kuchokera pakamwa pake,+ pakuti iye ndi mthenga wa Yehova wa makamu.+

  • Mateyu 13:52
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 Kenako anawauza kuti: “Popeza kuti zili choncho, mphunzitsi aliyense wa anthu akaphunzitsidwa za ufumu wakumwamba,+ amakhala ngati munthu, mwininyumba, amene amatulutsa zinthu zatsopano ndi zakale mosungiramo chuma chake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena