Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 31:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Ngati ndayesa golide chinthu chodalira,

      Kapena ngati ndanena kwa golide kuti, ‘Ndimadalira iwe,’+

  • Salimo 49:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Anthu amene akukhulupirira chuma chawo,+

      Amene akudzitamandira chifukwa cha kuchuluka kwa chuma chawo,+

  • Salimo 49:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti pa imfa yake sangatenge kena kalikonse.+

      Ulemerero wake sudzapita naye pamodzi.+

  • Yeremiya 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova wanena kuti: “Munthu wanzeru asadzitamande chifukwa cha nzeru zake.+ Munthu wamphamvu asadzitamande chifukwa cha mphamvu zake.+ Munthu wachuma asadzitamande chifukwa cha chuma chake.”+

  • Mateyu 23:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Aliyense wodzikweza adzatsitsidwa,+ koma aliyense wodzichepetsa adzakwezedwa.+

  • 1 Timoteyo 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Lamula achuma+ a m’nthawi* ino kuti asakhale odzikweza,+ ndiponso kuti asamadalire chuma chosadalirika,+ koma adalire Mulungu, amene amatipatsa mowolowa manja zinthu zonse kuti tisangalale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena