Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 27:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inetu sindingayerekeze n’komwe kunena kuti amuna inu ndinu olungama.+

      Mpaka ine kumwalira, sindidzasiya kukhala ndi mtima wosagawanika.+

  • Salimo 26:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma ine ndidzayenda mogwirizana ndi mtima wanga wosagawanika.+

      Ndiwomboleni+ ndi kundikomera mtima.+

  • Salimo 41:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma ine mwandichirikiza chifukwa cha mtima wanga wosagawanika,+

      Ndipo mudzandiika pamaso panu mpaka kalekale.+

  • Salimo 78:72
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 72 Iye anayamba kuwaweta malinga ndi mtima wake wosagawanika,+

      Ndipo anayamba kuwatsogolera mwaluso.+

  • Miyambo 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Wosauka amene akuyenda ndi mtima wosagawanika ali bwino kuposa munthu wa milomo yopotoka,+ komanso munthu wopusa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena