Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 5:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mawu a anthu ena otunga madzi anamveka pamalo otungira madzi,+

      Kumeneko anayamba kusimba ntchito zolungama za Yehova,+

      Anasimba ntchito zolungama za anthu ake okhala m’midzi ya Isiraeli.

      Atatero m’pamene anthu a Yehova anapita kumizinda.

  • Salimo 17:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Sonyezani kukoma mtima kosatha mwa kuchita zodabwitsa,+ inu Mpulumutsi wa anthu othawira kwa inu,

      Amene akuthawa anthu ogalukira dzanja lanu lamanja.+

  • Salimo 60:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kuti okondedwa anu apulumutsidwe,+

      Tipulumutseni ndi dzanja lanu lamanja ndi kutiyankha.+

  • Salimo 98:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova wachititsa chipulumutso chake kudziwika.+

      Chilungamo chake wachisonyeza ku mitundu ya anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena