Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndimaganiza kuti: Munthu+ ndani kuti muzimuganizira,+

      Ndipo mwana wa munthu wochokera kufumbi ndani kuti muzimusamalira?+

  • Salimo 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova ali m’kachisi wake wopatulika.+

      Yehova, mpando wake wachifumu uli kumwamba.+

      Maso ake amaona, maso ake owala amasanthula+ ana a anthu.

  • Salimo 33:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kuchokera kumalo achikhalire kumene iye amakhala,+

      Wayang’anitsitsa onse okhala padziko lapansi.

  • Salimo 102:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Iye wayang’ana pansi ali kumalo oyera, okwezeka,+

      Yehova wayang’ana dziko lapansi ali kumwambako,+

  • Yeremiya 16:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pakuti maso anga akuona njira zawo zonse. Anthuwo sanabisike kwa ine, ndipo zolakwa zawo sizinabisike pamaso panga.+

  • Yeremiya 23:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Kodi munthu aliyense angabisale m’malo obisika ine osamuona?”+ watero Yehova.

      “Kodi kumwamba kapena padziko lapansi, pali chilichonse chimene chingabisike kwa ine?”+ watero Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena