2 Samueli 17:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ukatero, tikamuukire kumene tikudziwa kuti tikhoza kum’peza,+ ndipo tikam’fikira ngati mmene mame+ amagwera pansi. Pamenepo sipadzakhala aliyense wopulumuka, iyeyo ngakhale amuna onse amene ali naye. Salimo 3:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Nyamukani,+ inu Yehova! Ndipulumutseni+ inu Mulungu wanga!+Pakuti mudzakantha adani anga onse pachibwano.+Mano a anthu oipa mudzawaphwanyaphwanya.+ Salimo 17:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Chifukwa cha anthu oipa amene akundipondereza.Adani a moyo wanga atsala pang’ono kundipeza.+ Salimo 59:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 59 Inu Mulungu wanga, ndilanditseni kwa adani anga.+Nditetezeni kwa anthu amene akundiukira.+ Salimo 140:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Inu Yehova, ndithandizeni kuti manja a munthu woipa asandikhudze.+Nditetezeni kwa munthu wochita zachiwawa.+Nditetezeni kwa anthu amene andikonzera chiwembu kuti andikankhe ndi kundigwetsa.+ Mateyu 6:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Musatilowetse m’mayesero,+ koma mutilanditse kwa woipayo.’+
12 Ukatero, tikamuukire kumene tikudziwa kuti tikhoza kum’peza,+ ndipo tikam’fikira ngati mmene mame+ amagwera pansi. Pamenepo sipadzakhala aliyense wopulumuka, iyeyo ngakhale amuna onse amene ali naye.
7 Nyamukani,+ inu Yehova! Ndipulumutseni+ inu Mulungu wanga!+Pakuti mudzakantha adani anga onse pachibwano.+Mano a anthu oipa mudzawaphwanyaphwanya.+
4 Inu Yehova, ndithandizeni kuti manja a munthu woipa asandikhudze.+Nditetezeni kwa munthu wochita zachiwawa.+Nditetezeni kwa anthu amene andikonzera chiwembu kuti andikankhe ndi kundigwetsa.+