Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 48:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Mngelo amene wakhala akundiwombola ku masoka anga onse,+ adalitse anyamatawa.+

      Dzina langa ndi mayina a makolo anga, Abulahamu ndi Isaki, apitirize kutchulidwa kudzela mwa anawa,+

      Komanso, anawa adzachulukane, adzakhale khamu la anthu padziko lapansi.”+

  • 2 Samueli 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma Davide anayankha Rekabu ndi m’bale wake Bana, ana a Rimoni Mbeeroti kuti: “Pali Yehova Mulungu wamoyo,+ amene anawombola+ moyo wanga+ m’masautso anga onse,+

  • Salimo 103:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Tamanda amene akuwombola moyo wako kudzenje,+

      Amene akukuveka kukoma mtima kosatha ndi chifundo ngati chisoti chachifumu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena