-
Salimo 17:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Mitima yawo siimva chisoni,*+
Ndipo amalankhula modzikuza ndi pakamwa pawo.+
-
Ezekieli 28:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 “Iwe mwana wa munthu, uza mtsogoleri wa Turo kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti:
“‘“Chifukwa chakuti wadzikuza mumtima mwako,+ ndipo ukunena kuti, ‘Ndine mulungu.+ Ndakhala pampando wa mulungu+ pakatikati pa nyanja,’+ ngakhale kuti ndiwe munthu wochokera kufumbi+ osati mulungu,+ ndipo umadziona ngati mulungu . . .
-
-
-