Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamenepo phiri la Sinai linafuka utsi ponseponse,+ chifukwa chakuti Yehova anatsikira paphiripo m’moto.+ Utsi wakewo unali kukwera kumwamba ngati utsi wa uvuni,+ ndipo phiri lonse linali kunjenjemera kwambiri.+

  • Yobu 36:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Iye wafumbata mphezi m’manja mwake,

      Ndipo amailamula kuti igwere woukira.+

  • Salimo 77:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Phokoso la bingu lanu linali ngati la mawilo a galeta.+

      Mphezi zinaunika padziko.+

      Ndipo dziko lapansi linagwedezeka ndi kuyamba kunjenjemera.+

  • Salimo 144:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ng’animitsani mphezi kuti muwabalalitse.+

      Tumizani mivi yanu kuti muwasokoneze.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena