Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Anayamba kuponya mivi kuti awabalalitse.+

      Anaponya mphezi kuti awasokoneze.+

  • Yobu 36:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Iye wafumbata mphezi m’manja mwake,

      Ndipo amailamula kuti igwere woukira.+

  • Salimo 18:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Anayamba kuponya mivi kuti awabalalitse.+

      Anaponya mphezi kuti awasokoneze.+

  • Salimo 77:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Phokoso la bingu lanu linali ngati la mawilo a galeta.+

      Mphezi zinaunika padziko.+

      Ndipo dziko lapansi linagwedezeka ndi kuyamba kunjenjemera.+

  • Salimo 97:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mphezi zake zinawalitsa dziko lapansi.+

      Dziko linaona ndipo linachita mantha kwambiri.+

  • Zekariya 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Zidzakhala zoonekeratu kuti Yehova ali ndi anthu ake,+ ndipo muvi wake udzathamanga ngati mphezi.+ Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa adzaliza lipenga lanyanga ya nkhosa,+ ndipo adzapita ndi mphepo yamkuntho ya kum’mwera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena