Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu Yehova, nditsogolereni m’chilungamo chanu+ chifukwa adani anga andizungulira.+

      Salazani njira yanu kuti ndiyendemo popanda chopunthwitsa.+

  • Salimo 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye adzaweruza anthu padziko lapansi mwachilungamo.+

      Adzazenga mlandu mitundu ya anthu moyenerera.+

  • Salimo 71:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mundilanditse chifukwa cha chilungamo chanu ndipo mundipulumutse.+

      Tcherani khutu lanu kwa ine ndi kundipulumutsa.+

  • Salimo 146:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye ndi Woperekera chiweruzo anthu ochitiridwa chinyengo,+

      Wopereka chakudya kwa anthu anjala.+

      Yehova amamasula anthu omangidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena