Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 inuyo mumve muli kumwamba pemphero lawo ndi pempho lawo lopempha chifundo, ndipo muonetsetse kuti chilungamo chachitika kwa iwo.+

  • Salimo 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndidzafuulira Yehova mokweza,

      Ndipo iye adzandiyankha m’phiri lake loyera.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 46:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Mulungu ndiye pothawira pathu ndi mphamvu yathu,+

      Thandizo lopezeka mosavuta pa nthawi ya masautso.+

  • Yesaya 41:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti ine, Yehova Mulungu wako, ndagwira dzanja lako lamanja.+ Ine amene ndikukuuza kuti, ‘Usachite mantha.+ Ineyo ndikuthandiza.’+

  • Yeremiya 20:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma Yehova anali nane+ ngati msilikali wamphamvu ndi woopsa.+ N’chifukwa chake anthu amene akundizunza adzakhumudwa ndipo sadzapambana.+ Adzachita manyazi kwambiri chifukwa adzaona kuti sizinawayendere bwino. Manyazi awo adzakhala nawo mpaka kalekale ndipo sadzaiwalika.+

  • Danieli 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Danieli atangodziwa kuti lamulo limeneli lasainidwa, analowa m’nyumba mwake, ndipo mawindo a nyumba yake oyang’ana ku Yerusalemu+ anali otsegula. M’nyumbamo, iye anali kugwada ndi kupemphera+ kwa Mulungu wake ndi kumutamanda+ katatu pa tsiku,+ monga mmene anali kuchitira nthawi zonse lamuloli lisanasainidwe.+

  • Aheberi 13:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Moti tikhale olimba mtima ndithu+ ndipo tinene kuti: “Yehova* ndiye mthandizi wanga. Sindidzaopa. Munthu angandichite chiyani?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena