Salimo 18:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Zingwe za Manda zinandizungulira.+Ndinayang’anizana ndi misampha ya imfa.+ Salimo 25:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Masautso a mtima wanga awonjezeka.+Ndilanditseni ku nkhawa zimene zili pa ine.+ Salimo 40:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Iye ananditulutsanso m’dzenje la madzi a mkokomo,+Ananditulutsa m’chithaphwi cha matope.+Kenako anapondetsa phazi langa pathanthwe.+Anandiyendetsa panthaka yolimba.+ Salimo 71:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Chifukwa chakuti mwandionetsa masautso ndi masoka ambiri,+Nditsitsimutseni.+Nditulutseninso m’madzi akuya, pansi pa nthaka.+ Maliro 3:55 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 55 Inu Yehova, ndaitana dzina lanu mofuula ndili m’dzenje lakuya kwambiri.+ Yona 2:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 kuti:“Pamene ndinali m’masautso ndinaitana Yehova,+ ndipo anandiyankha.+Ndinafuula kupempha thandizo ndili m’Manda* akuya.+Ndipo inu munamva mawu anga.+ Aheberi 5:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Pamene anali munthu, Khristu anapereka mapemphero opembedzera ndi opempha,+ kwa amene anali wokhoza kumupulumutsa ku imfa. Anapereka mapempherowa mofuula+ komanso akugwetsa misozi, ndipo anamumvera chifukwa chakuti anali kuopa Mulungu.+
2 Iye ananditulutsanso m’dzenje la madzi a mkokomo,+Ananditulutsa m’chithaphwi cha matope.+Kenako anapondetsa phazi langa pathanthwe.+Anandiyendetsa panthaka yolimba.+
20 Chifukwa chakuti mwandionetsa masautso ndi masoka ambiri,+Nditsitsimutseni.+Nditulutseninso m’madzi akuya, pansi pa nthaka.+
2 kuti:“Pamene ndinali m’masautso ndinaitana Yehova,+ ndipo anandiyankha.+Ndinafuula kupempha thandizo ndili m’Manda* akuya.+Ndipo inu munamva mawu anga.+
7 Pamene anali munthu, Khristu anapereka mapemphero opembedzera ndi opempha,+ kwa amene anali wokhoza kumupulumutsa ku imfa. Anapereka mapempherowa mofuula+ komanso akugwetsa misozi, ndipo anamumvera chifukwa chakuti anali kuopa Mulungu.+