Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 65:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Malo odyetserako ziweto a m’chipululu akukha mafuta,+

      Ndipo zitunda zamangirira chisangalalo m’chiuno mwawo.+

  • Salimo 98:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Mitsinje iwombe m’manja,

      Mapiri onse afuule pamodzi mokondwera pamaso pa Yehova.+

  • Yesaya 44:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Fuulani mokondwa kumwamba inu,+ pakuti Yehova wachitapo kanthu.+ Fuulani mosangalala,+ inu malo otsika kwambiri a dziko lapansi.+ Mapiri+ inu ndiponso iwe nkhalango ndi inu mitengo yonse ili mmenemo, kondwani ndi kufuula ndi chisangalalo. Pakuti Yehova wawombola Yakobo ndipo wasonyeza kukongola kwake pa Isiraeli.”+

  • Yesaya 49:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Fuulani mokondwa kumwamba inu,+ ndipo sangalala iwe dziko lapansi.+ Mapiri asangalale ndipo afuule ndi chisangalalo.+ Pakuti Yehova watonthoza anthu ake+ ndipo amamvera chisoni anthu ake osautsidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena