Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 13:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pamapeto pake Abisalomu anati: “Ngati inuyo simubwera, chonde lolani kuti Aminoni m’bale wanga apite nafe.”+ Pamenepo mfumu inamufunsa kuti: “N’chifukwa chiyani ukufuna kuti apite nawe?”

  • Salimo 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iwo amalankhulana zabodza.+

      Amalankhulana ndi milomo yoshashalika+ komanso ndi mitima iwiri.+

  • Salimo 28:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Musandikokolole pamodzi ndi anthu oipa komanso anthu amene amachita zopweteka anzawo,+

      Anthu amene amalankhula mawu amtendere ndi anzawo+ koma m’mitima yawo muli zinthu zoipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena