Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 5:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti m’kamwa mwawo simutuluka mawu okhulupirika.+

      Mitima yawo yadzaza ndi zinthu zoipa.+

      Mmero wawo ndi manda otseguka.+

      Iwo amalankhula ndi lilime lachinyengo.+

  • Salimo 28:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Musandikokolole pamodzi ndi anthu oipa komanso anthu amene amachita zopweteka anzawo,+

      Anthu amene amalankhula mawu amtendere ndi anzawo+ koma m’mitima yawo muli zinthu zoipa.+

  • Salimo 62:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iwo amapatsa munthu malangizo kuti amukope ndi kumutsitsa pamalo ake aulemu.+

      Bodza limawasangalatsa.+

      Iwo amadalitsa ndi pakamwa pawo, koma mumtima mwawo amatemberera.+ [Seʹlah.]

  • Yeremiya 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Lilime lawo ndiwo muvi wophera anthu.+ Limalankhula chinyengo chokhachokha. Munthu aliyense amalankhula mwamtendere ndi mnzake, koma mumtima mwake amakonza chiwembu.”+

  • Aroma 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti anthu oterowo si akapolo a Ambuye wathu Khristu, koma a mimba zawo.+ Ndipo mwa kulankhula mawu okopa+ ndi achinyengo+ amanyenga anthu oona mtima.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena