Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 6:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 “Tsopano Mulungu wanga, chonde, maso anu aone,+ ndipo makutu anu+ akhale tcheru kumvetsera pemphero lokhudza malo ano.

  • Salimo 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ine ndikuitana pa inu, chifukwa mudzandiyankha, inu Mulungu.+

      Tcherani khutu kwa ine. Imvani mawu anga.+

  • Salimo 65:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Inu Wakumva pemphero, anthu a mitundu yonse adzabwera kwa inu.+

  • Salimo 71:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mundilanditse chifukwa cha chilungamo chanu ndipo mundipulumutse.+

      Tcherani khutu lanu kwa ine ndi kundipulumutsa.+

  • Salimo 130:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Imvani mawu anga Yehova.+

      Makutu anu amve mawu anga ochonderera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena