Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 4:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Mayiyo atafika kwa munthu wa Mulungu woona paphiripo, nthawi yomweyo anam’gwira mapazi.+ Gehazi ataona zimenezo, anabwera pafupi kuti am’kankhe mayiyo.+ Koma munthu wa Mulungu woonayo+ anamuuza kuti: “Musiye,+ mtima wake ukum’pweteka kwambiri.+ Koma Yehova wandibisira,+ sanandiuze.”

  • Yobu 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Choncho, ine sinditseka pakamwa panga.

      Ndilankhula chifukwa cha kuvutika mumtima,+

      Ndilankhula za nkhawa zanga, chifukwa moyo wanga ukupweteka.

  • Yobu 21:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Winanso adzafa ali wokwiya,

      Asanadye zinthu zabwino.+

  • Luka 22:62
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Ndipo anatuluka panja ndi kuyamba kulira mopwetekedwa mtima kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena