Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 2:58
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 58 Anetini+ onse pamodzi ndi ana a atumiki a Solomo analipo 392.+

  • Nehemiya 11:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anetini+ anali kukhala ku Ofeli,+ ndipo Ziha ndi Gisipa anali kuyang’anira Anetiniwo.

  • Esitere 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 M’zigawo zonse ndi m’mizinda yonse kumene mawu a mfumu ndi lamulo lake linafika, Ayuda anali kusangalala ndi kukondwera. Anachita phwando+ ndipo linali tsiku lachisangalalo. Anthu ambiri+ a m’dzikomo anayamba kudzitcha Ayuda+ chifukwa anali kuchita mantha kwambiri+ ndi Ayudawo.

  • Yesaya 56:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Alendo amene adziphatika kwa Yehova kuti am’tumikire+ ndiponso amene amakonda dzina la Yehova+ n’cholinga choti akhale atumiki ake, onse amene amasunga sabata kuti asalidetse ndiponso amene amatsatira pangano langa,+

  • Yesaya 60:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mitundu ya anthu idzatsata kuwala kwako,+ ndipo mafumu+ adzatsata kunyezimira kwako.+

  • Zekariya 8:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Anthu ambiri a mitundu ina ndiponso mitundu yamphamvu ya anthu idzabweradi kudzafunafuna Yehova wa makamu mu Yerusalemu.+ Idzabwera kudzakhazika pansi mtima wa Yehova.’

  • Zekariya 8:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Yehova wa makamu wanena kuti, ‘M’masiku amenewo, amuna 10 ochokera m’zilankhulo zonse za anthu a mitundu ina+ adzagwira+ chovala cha munthu amene ndi Myuda+ ndi kunena kuti: “Anthu inu tipita nanu limodzi,+ chifukwa tamva kuti Mulungu ali ndi inu.”’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena